Mateyu 9:35 BL92

35 Ndipo Yesu anayendayenda m'mizinda yonse ndi m'midzi, namaphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira uthenga wabwino wa Ufumuwo, naciritsa nthenda iri yonse ndi zofoka zonse.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 9

Onani Mateyu 9:35 nkhani