21 Ndipo Yehu anatumiza kwa Aisrayeti onse, nadza otumikira Baala onse, wosatsala ndi mmodzi yense wosafika. Nalowa m'nyumba ya Baala; ndi nyumba ya Baala inadzala pha.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10
Onani 2 Mafumu 10:21 nkhani