2 Mafumu 11:14 BL92

14 napenya, ndipo taonani, mfumu iri ciriri paciundo, monga adafocita, ndi atsogoleri ndi amalipenga pali mfomu; nakondwerera anthu onse a m'dziko, naomba malipenga. Pamenepo Ataliya anang'amba zobvala zace, napfuula, Ciwembu, Ciwembu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 11

Onani 2 Mafumu 11:14 nkhani