2 Mafumu 12:7 BL92

7 Pamenepo mfumu Yoasi anaitana Yehoyada wansembe, ndi ansembe ena, nanena nao, Mulekeranji kukonza mogamuka nyumba? Tsono musalandiranso ndarama kwa anzanu odziwana nao, kuziperekera mogamuka nyumba.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 12

Onani 2 Mafumu 12:7 nkhani