2 Mafumu 14:11 BL92

11 Koma Amaziya sanamvera. Motero anakwera Yoasi mfumu ya Israyeli, ndipo iye ndi Amaziya mfumu ya Yuda anapenyana maso ku Betisemesi, ndiwo wa Yuda.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 14

Onani 2 Mafumu 14:11 nkhani