2 Mafumu 16:18 BL92

18 Nacotsa ku nyumba ya Yehova malo ophimbika a pa Sabata adawamanga kunyumba, ndi polowera mfumu pofuma kunja, cifukwa ca mfumu ya Asuri.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 16

Onani 2 Mafumu 16:18 nkhani