15 Nati iye, Anaona ciani m'nyumba mwanu? Nati Hezekiya, Zonse za m'nyumba mwanga anaziona, palibe kanthu pacuma canga kosawaonetsa.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 20
Onani 2 Mafumu 20:15 nkhani