2 Mafumu 22:17 BL92

17 popeza anandisiya Ine, nafukizira zonunkhira milungu yina, kuti autse mkwiyo wanga ndi nchito zonse za manja ao; cifukwa cace mkwiyo wanga udzayakira malo ana wosazimikanso.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 22

Onani 2 Mafumu 22:17 nkhani