2 Mafumu 22:19 BL92

19 popeza mtima wako ngoolowa, ndipo unadzicepetsa pamaso pa Yehova muja udamva zonenera Ine malo ana ndi anthu okhalamo, kuti adzakhala abwinja, ndi temberero; ndipo unang'amba zobvala zako ndi kulira misozi pamaso panga, Inenso ndakumvera, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 22

Onani 2 Mafumu 22:19 nkhani