2 Mafumu 23:27 BL92

27 Nati Yehova, Ndidzacotsa Yudanso pamaso panga, monga umo ndinacotsera Israyeli; ndipo ndidzataya mudzi uwu ndidausankha, ndiwo Yerusalemu, ndi nyumba ndidainena, Dzina langa lidzakhala komweko.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 23

Onani 2 Mafumu 23:27 nkhani