4 Ndipo Mesa mfumu ya Moabu anali mwini nkhosa, akapereka kwa mfumu ya Israyeli ubweya wa ana a nkhosa zikwi zana limodzi, ndi wa mphongo zikwi zana limodzi.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 3
Onani 2 Mafumu 3:4 nkhani