11 Koma mtima wa mfumu ya Aramu unabvutika kwambiri pa icico, naitana anyamata ace, nanena nao, Kodi simudzandiuza wina wa ife wobvomerezana ndi mfumu ya Israyeli ndani?
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6
Onani 2 Mafumu 6:11 nkhani