18 Ndipo atatsikira pali iye, Elisa anapemphera kwa Yehova, nati, Mukanthe mtundu uwu ucite khungu. Ndipo iye anawakantha, nawacititsa khungu, monga mwa mau a Elisa.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6
Onani 2 Mafumu 6:18 nkhani