2 Mafumu 7:5 BL92

5 Nanyamuka iwo kuli sisiro kukalowa ku misasa ya Aaramu; koma pofika polekezera pace pa misasa ya Aaramu, taonani, panalibe munthu pomwepo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 7

Onani 2 Mafumu 7:5 nkhani