22 Ndipo kunali, pamene Yoramu anaona Yehu, anari, Mtendere kodi, Yehu? Nati iye, Ngwanji mtendere pokhala cacuruka cigololo ndi nyanga zace za mai wako Yezebeli?
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9
Onani 2 Mafumu 9:22 nkhani