26 Ndapenyadi dzulo mwazi wa Naboti ndi mwazi wa ana ace, ati Yehova; ndipo ndikubwezera pamunda pano, ati Yehova, Mtengeni tsono, mumponye pamundapo, monga mwa mau a Yehova.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9
Onani 2 Mafumu 9:26 nkhani