Mateyu 10:16 BL92

16 Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa afisi; cifukwa cace khalani ocenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 10

Onani Mateyu 10:16 nkhani