11 Indetu ndinena kwa inu, Sanauke wakubadwa mwa akazi munthu wamkuru woposa Yohane Mbatizi; koma iye amene ali wocepa mu Ufumu wa Kumwamba amkulira iye.
Werengani mutu wathunthu Mateyu 11
Onani Mateyu 11:11 nkhani