Mateyu 11:19 BL92

19 Mwana wa munthu anadza wakudya, ndi wakumwa, ndipo iwo amati, Onani munthu wakudyaidya ndi wakumwaimwa vinyo, bwenzi la amisonkho ndi ocimwa! Ndipo nzeru iyesedwa yolungama ndi nchito zace.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 11

Onani Mateyu 11:19 nkhani