Mateyu 11:21 BL92

21 Tsoka kwa iwe, Korazini! tsoka kwa iwe, Betsaida! cifukwa ngati zamphamvu zimene zacitidwa mwa inu zikadacitidwa m'Turo ndi m'Sidoni, akadatembenuka mtima kale kale m'ziguduli ndi m'phulusa.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 11

Onani Mateyu 11:21 nkhani