Mateyu 11:23 BL92

23 Ndipo iwe, Kapernao, udzakwezedwa kodi kufikira kuthambo? udzatsika kufikira ku dziko la akufa: cifukwa ngati zamphamvu zimene zacitidwa mwa iwe zikadacitidwa m'Sodomu, uyo ukadakhala kufikira lero.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 11

Onani Mateyu 11:23 nkhani