Mateyu 12:42 BL92

42 3 Mfumu yaikazi ya kumwera adzauka pamlandu pamodzi ndi obadwa amakono, nadzawatsutsa; cifukwa iye anacokera ku mathero a dziko lapansi kudzamva nzeru ya Solomo; ndipo onani, wakuposa Solomo ali pano.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 12

Onani Mateyu 12:42 nkhani