Mateyu 12:41 BL92

41 1 Anthu a ku Nineve adzauka pamlandu pamodzi ndi obadwa amakono, nadzawatsutsa; cifukwa 2 iwo anatembenuka mtima ndi kulalikira kwace kwa Yona; ndipo onani, wakuposa Y ona ali pano.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 12

Onani Mateyu 12:41 nkhani