Mateyu 13:15 BL92

15 Cifukwa unalemera mtima wa anthuawa,Ndipo m'makutu ao anamva mogontha,Ndipo maso ao anatsinzina;Kuti asaone konse ndi maso,Asamve ndi makutu,Asazindikire ndi mtima wao,Asatembenuke,Ndipo ndisawaciritse iwo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:15 nkhani