Mateyu 13:23 BL92

23 Ndipo iye amene afesedwa pa nthaka yabwino, uyu ndiye wakumva mau nawadziwitsa; amene abaladi zipatso, nazifitsa, ena za makumi khumi, ena za makumi asanu ndi limodzi, ena za makumi atatu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:23 nkhani