Mateyu 13:22 BL92

22 Ndipo iye amene afesedwa kuminga, uyu ndiye wakumva mau; ndipo kulabadira kwa dziko lapansi, ndi cinyengo ca cuma citsamwitsa mau, ndipo akhala wopanda cipatso.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:22 nkhani