Mateyu 13:27 BL92

27 Ndipo anyamata ace a mwini nyumbayo anadza, nati kwa iye, Mbuye, kodi simunafesa mbeu zabwino m'munda mwanu? nanga wacokera kuti namsongoleyo?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:27 nkhani