Mateyu 13:28 BL92

28 Ndipo iye ananena kwa iwo, Munthu mdani wanga wacicita ici. Ndipo anyamata anati kwa iye, Kodi mufuna tsopano kuti timuke, tikamsonkhanitse uyo pamodzi?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:28 nkhani