Mateyu 13:32 BL92

32 kamene kakhaladi kakang'ono koposa mbeu zonse, koma katakula, kali kakakuru kuposa zitsambazonse, nukhala mtengo, kotero kuti mbalame za mlengalenga zimadza, nizibindikira mu nthambi zace.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:32 nkhani