Mateyu 14:15 BL92

15 Ndipo pamene panali madzulo, ophunzira ace anafika kwa Iye, nanena, Malo ano nga cipululu, ndipo nthawi yapita tsopano; kauzeni makamuwo amuke, apite ku midzi kukadzigulira okha kamba.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 14

Onani Mateyu 14:15 nkhani