Mateyu 15:28 BL92

28 Pomwepo Yesu anayankha, nati kwa iye, Mkaziwe, cikhulupiriro cako ndi cacikuru; cikhale kwa iwe monga momwe wafunira. Ndipo mwana wace anacira nthawi yomweyo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 15

Onani Mateyu 15:28 nkhani