Mateyu 17:4 BL92

4 Ndipo Petro anayankha, nati kwa Yesu, Ambuye, kuli bwino kuti ife tikhale pano; ngati mulola ndidzamanga pane misasa itatu; umodzi wa Inu, ndi wina wa Mose, ndi wina wa Eliya.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 17

Onani Mateyu 17:4 nkhani