Mateyu 17:5 BL92

5 Akali cilankhulire, onani, mtambo wowala unawaphi mba iwo: ndipo onani, mau alikunena mumtambo, Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa, mwa iyeyu ndikondwera, mverani Iye.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 17

Onani Mateyu 17:5 nkhani