Mateyu 19:8 BL92

8 Iye ananena kwa iwo, Cifukwa ca kuuma mtima kwanu, Mose anakulolezani kucotsa akazi anu; koma paciyambi sikunakhala comweco.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 19

Onani Mateyu 19:8 nkhani