Mateyu 19:9 BL92

9 Ndipo Ine ndinena kwa inu, Amene ali yense akacotsa mkazi wace, kosakhala cifukwa ca cigololo, nadzakwatira wina, acita cigololo: ndipo iye amene akwatira wocotsedwayo, acita cigololo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 19

Onani Mateyu 19:9 nkhani