Mateyu 20:30 BL92

30 Ndipo onani, anthu akhungu awiri anakhala m'rnphepete mwa njira; m'mene iwo anamva kuti Yesu analikupitirirapo, anapfuula nati, Muticitire ife cifundo, Inu Mwana wa Davide.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 20

Onani Mateyu 20:30 nkhani