Mateyu 20:31 BL92

31 Ndipo khamulo linawaletsa, kuti atonthole: koma anakuwitsa, nanena, Ambuye, muticitire cifundo, Inu Mwana wa Davide.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 20

Onani Mateyu 20:31 nkhani