Mateyu 21:16 BL92

16 nanena kwa Iye, Mulinkumva kodi cimene alikunena awa? Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Inde: simunawerenga kodi, M'kamwa mwa makanda ndi oyamwa munafotokozera zolemekeza?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 21

Onani Mateyu 21:16 nkhani