Mateyu 21:33 BL92

33 Mverani fanizo lina: Panali munthu, mwini banja, amene analima munda wamphesa, nauzunguniza linga, nakumba umo moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 21

Onani Mateyu 21:33 nkhani