Mateyu 22:4 BL92

4 Pomwepo anatumizanso akapolo ena, nanena, Uzani oitanidwawo, Onani, ndakonza phwando langa; ng'ombe zanga, ndi zonona ndinazipha, ndi zinthu zonse zapsya: idzani kuukwati.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 22

Onani Mateyu 22:4 nkhani