Mateyu 23:25 BL92

25 Tsoka inu, alembi ndi Afarisi, onyenga! cifukwa mutsuka kunja kwace kwa cikho ndi mbale, koma m'katimo iwo adzala ndi kulanda ndi kusadziletsa.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 23

Onani Mateyu 23:25 nkhani