Mateyu 24:3 BL92

3 Ndipo pamene Iye analikukhala pansi pa phiri la Azitona, ophunzira anadza kwa Iye pa yekha, nanena, Mutiuze ife zija zidzaoneka liti? ndipo cizindikiro ca kufika kwanu nciani, ndi ca mathedwe a nthawi ya pansi pano?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 24

Onani Mateyu 24:3 nkhani