Mateyu 5:13 BL92

13 Inu ndinu mcere wa dziko lapansi; koma mcerewo ngati uka: sukuluka, adzaukoleretsa ndi ciani? Pamenepo sungakwanirenso kanthu konse, koma kuti ukaponyedwe kunja, nupondedwe ndi anthu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 5

Onani Mateyu 5:13 nkhani