Mateyu 6:26 BL92

26 Yang'anirani mbalame za kumwamba, kuti sizimafesa ai, kapena sizimatema ai, kapena sizimatutira m'nkhokwe; ndipo Atate wanu wa Kumwamba azidyetsa. Nanga inu mulibe kusiyana nazo kuziposa kodi?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:26 nkhani