Mateyu 6:25 BL92

25 Cifukwa cace ndinena kwa inu, Musadere nkhawa moyo wanu, cimene mudzadya ndi cimene mudzamwa; kapena thupi lanu, cimene mudzabvala. Kodi moyo suli woposa cakudya, ndi thupi loposa cobvala?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:25 nkhani