Mateyu 6:24 BL92

24 Palibe munthu angathe kukhala kapolo wa ambuye awiri: pakuti pena adzamuda mmodziyo, ndi kukonda winayo; pena adzakangamira kwa mmodzi, nadzanyoza wina. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Cuma.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:24 nkhani