Mateyu 8:16 BL92

16 Ndipo pakudza madzulo, anabwera nao kwa Iye anthu ambiri ogwidwa ndi mizimu yoipa; ndipo Iye anaturutsa mizimuyo ndi mau, naciritsa akudwala onse;

Werengani mutu wathunthu Mateyu 8

Onani Mateyu 8:16 nkhani