Mateyu 9:18 BL92

18 M'mene Iye analikulankhula nao zinthu zimenezo, onani, anadza munthu mkuru, namgwadira Iye, nanena, Wamwalira tsopanolimwana wanga wamkazi, komatu mudze muike dzanja lanu pa iye, ndipo adzakhala ndi moyo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 9

Onani Mateyu 9:18 nkhani