Mateyu 9:17 BL92

17 Kapena samathira vinyo watsopano m'matumba akale; akatero, matumba aphulika, ndi vinyo atayika, ndi matumba aonongeka: koma athira vinyo watsopano m'matumba atsopano, ndi zonse ziwiri zisungika.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 9

Onani Mateyu 9:17 nkhani