2 Mafumu 1:17 BL92

17 Motero anafa monga mwa mau a Yehova adanena Eliyawo. Ndipo Yehoramu analowa ufumu m'malo mwace caka caciwiri ca Yehoramu mwana wa Yehosafati mfumu ya Yuda, pakuti analibe mwana wamwamuna.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 1

Onani 2 Mafumu 1:17 nkhani